Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Nehemiya 10:10 - Buku Lopatulika

ndi abale ao: Sebaniya, Hodiya, Kelita, Pelaya, Hanani,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi abale ao: Sebaniya, Hodiya, Kelita, Pelaya, Hanani,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

ndi abale ao aŵa: Sebaniya, Hodiya, Kelita, Pelaya, Hanani,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ndi abale awo awa: Sebaniya, Hodiya, Kelita, Pelaya, Hanani,

Onani mutuwo



Nehemiya 10:10
10 Mawu Ofanana  

Ndi ana a mkazi wa Hodiya, mlongo wake wa Nahamu, ndiwo atate a Keila Mgarimi ndi Esitemowa Mmaaka.


Ndi a Alevi: Yozabadi, ndi Simei, ndi Kelaya (ndiye Kelita), Petahiya, Yuda, ndi Eliyezere.


Ndipo pa tsiku lachinai siliva ndi golide ndi zipangizo zinayesedwa m'nyumba ya Mulungu wathu, m'dzanja la Meremoti mwana wa Uriya wansembe, ndi pamodzi naye Eleazara mwana wa Finehasi, ndi pamodzi nao Yozabadi mwana wa Yesuwa, ndi Nowadiya mwana wa Binuyi, Alevi;


Mika, Rehobu, Hasabiya,


Ndi Alevi ndiwo Yesuwa mwana wa Azaniya, Binuyi wa ana a Henadadi, Kadimiyele;


Ndi Alevi ndiwo Yesuwa, Binuyi, Kadimiyele, Serebiya, Yuda, ndi Mataniya; iye ndi abale ake amatsogolera mayamiko.


Potsatizana naye Binuyi mwana wa Henadadi anakonza gawo lina, kuyambira kunyumba ya Azariya kufikira popindirira kufikira kungodya.


A Levi: ana a Yesuwa, a Kadimiyele, a ana a Hodeva, makumi asanu ndi awiri kudza anai.


Ndi Yesuwa, ndi Bani, ndi Serebiya, Yamini, Akubu, Sabetai, Hodiya, Maaseiya, Kelita, Azariya, Yozabadi, Hanani, Pelaya, ndi Alevi, anadziwitsa anthu chilamulocho; ndi anthu anali chilili pamalo pao.