Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mlaliki 8:2 - Buku Lopatulika

Nditi, Sunga mau a mfumu, makamaka m'kulumbira Mulungu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nditi, Sunga mau a mfumu, makamaka m'kulumbira Mulungu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Uzimvera lamulo la mfumu, ndipo chifukwa cha lumbiro lako kwa Mulungu usade nkhaŵa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ine ndikuti, mvera lamulo la mfumu, chifukwa unalumbira pamaso pa Mulungu.

Onani mutuwo



Mlaliki 8:2
10 Mawu Ofanana  

Koma mfumu inaleka Mefiboseti mwana wa Yonatani, mwana wa Saulo, chifukwa cha lumbiro la kwa Yehova linali pakati pa Davide ndi Yonatani mwana wa Saulo.


Sunasunga chifukwa ninji lumbiro la pa Yehova, ndi lamulo lija ndinakulamulira iwe?


Ndi akulu onse, ndi amuna amphamvu onse, ndi ana aamuna onse omwe a mfumu Davide, anagonjeratu kwa Solomoni mfumu.


lumbiro la Yehova likhale pakati pa iwo awiri, kuti sanatulutse dzanja lake pa chuma cha mnansi wake; ndipo mwiniyo azivomereza, ndipo asalipe.


Mwananga, opa Yehova ndi mfumu yomwe, osadudukira anthu osinthasintha.


Uwakumbutse iwo agonje kwa akulu, ndi aulamuliro, akhale omvera, okonzeka pa ntchito iliyonse yabwino;


Ndipo pakufika anthuwo m'nkhalangomo, onani, madzi a uchi anachuluka; koma panalibe munthu mmodzi anaika dzanja lake pakamwa, pakuti anthuwo anaopa tembererolo.