Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mlaliki 4:6 - Buku Lopatulika

Dzanja limodzi lodzala pali mtendere liposa manja awiri oti thoo pali vuto ndi kungosautsa mtima.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Dzanja limodzi lodzala pali mtendere liposa manja awiri oti thoo pali vuto ndi kungosautsa mtima.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Komabe nkwabwino kukhala ndi moyo wabata wodzaza dzanja limodzi, kupambana kutekeseka ndi ntchito zolemetsa zodzaza manja aŵiri, ndipo kuyesa kuzimvetsa nkungozivuta chabe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Nʼkwabwino kukhala ndi dzanja limodzi lodzaza uli pa mtendere, kuposa kukhala ndi manja awiri odzaza uli pa mavuto, ndipo uku nʼkungodzivuta chabe.

Onani mutuwo



Mlaliki 4:6
7 Mawu Ofanana  

Zochepa zake za wolungama zikoma koposa kuchuluka kwao kwa oipa ambiri.


Zapang'ono, pokhala chilungamo, ziposa phindu lalikulu lopanda chiweruzo.


Nyenyeswa youma, pokhala mtendere, iposa nyumba yodzala nyama yansembe, pali makangano.


Ndaona ntchito zonse zipangidwa kunja kuno; ndipo zonsezo ndi chabe ndi kungosautsa mtima.


Ndipo ndinapereka mtima kudziwa nzeru ndi kudziwa misala ndi utsiru; ndinazindikira kuti ichinso chingosautsa mtima.


Pamenepo ndinabwera ndi kupenyera zachabe kunja kuno.