Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mlaliki 3:9 - Buku Lopatulika

Wogwira Ntchito aona phindu lanji m'chomsautsacho?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Wogwira Ntchito aona phindu lanji m'chomsautsacho?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kodi wantchito amapeza phindu lanji pa ntchito yake yolemetsa?

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kodi wantchito amapeza phindu lanji pa ntchito yake yolemetsa?

Onani mutuwo



Mlaliki 3:9
7 Mawu Ofanana  

M'ntchito zonse muli phindu; koma kulankhulalankhula kungopatsa umphawi.


Kodi ntchito zake zonse munthu asauka nazo zimpindulira chiyani?


Pamenepo ndinayang'ana zonse manja anga anazipanga, ndi ntchito zonse ndinasauka pozigwira; ndipo taona, zonse zinali zachabechabe ndi kungosautsa mtima, ndipo kunalibe phindu kunja kuno.


Ichinso ndi choipa chowawa, chakuti adzangopita monse monga anadza; ndipo wodzisautsa chabe adzaona phindu lanji?


Pakuti munthu adzapindulanji, akalandira dziko lonse, nataya moyo wake? Kapena munthu adzaperekanji chosintha ndi moyo wake?


kuti inunso muvomere otere, ndi yense wakuchita nao, ndi kugwiritsa ntchito.