Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mlaliki 2:2 - Buku Lopatulika

Ndinati, Kuseka ndi masala; ndi chimwemwe kodi chichita chiyani?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndinati, Kuseka ndi masala; ndi chimwemwe kodi chichita chiyani?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kukakhala kuseka, ndidati, “Imene ija ndi misala.” Chikakhala chisangalatso, ndidati, “Phindu lake nchiyani?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Kuseka,” ndinati, “imeneyo ndi misala. Ndipo kodi chisangalalo chimabweretsa phindu lanji?”

Onani mutuwo



Mlaliki 2:2
6 Mawu Ofanana  

Ngakhale m'kuseka mtima uwawa; ndipo matsiriziro a chiphwete ndi chisoni.


Mtima wosekerera uchiritsa bwino; koma mzimu wosweka uphwetsa mafupa.