Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mlaliki 10:9 - Buku Lopatulika

Wosendeza miyala adzaphwetekedwa nayo; wowaza nkhuni nadzitema.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Wosendeza miyala adzaphwetekedwa nayo; wowaza nkhuni nadzitema.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Amene amakumba miyala, itha kumpweteka miyalayo. Amene amaŵaza nkhuni, atha kudzipweteka nazo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Amene amaphwanya miyala adzapwetekedwa ndi miyalayo; amene amawaza nkhuni adzapwetekedwa nazo.

Onani mutuwo



Mlaliki 10:9
2 Mawu Ofanana  

Chitsulo chikakhala chosathwa, ndipo ukaleka kunola, uzipambana kulimbikira; koma nzeru ipindulira pochenjeza.


Wokumba mbuna adzagwamo; ndipo woboola mpanda njoka idzamluma.