Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mlaliki 10:7 - Buku Lopatulika

Ndaona akapolo atakwera pa akavalo, ndi mafumu, alikuyenda pansi ngati akapolo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndaona akapolo atakwera pa akavalo, ndi mafumu, alikuyenda pansi ngati akopolo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndaona akapolo akuyenda pa akavalo, m'menemo akalonga akuyenda pansi ngati akapolo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndaona akapolo atakwera pa akavalo, pamene akalonga akuyenda pansi ngati akapolo.

Onani mutuwo



Mlaliki 10:7
4 Mawu Ofanana  

Ndipo mfumu inatuluka, ndi anthu onse anamtsata; naima kunyumba ya pa yokha.


amtengere chovala chachifumu amachivala mfumu, ndi kavalo amakwerapo mfumu, naike korona wachifumu pamutu pake,


Wopusa sayenera kukhala ndi zinthu zolongosoka; nanga kapolo ayenera kulamulira akalonga kodi?


chifukwa cha kapolo pamene ali mfumu; ndi chitsiru chitakhuta zakudya;