Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mlaliki 10:4 - Buku Lopatulika

Ngati mkulu akukwiyira, usasiye malo ako; chifukwa chifatso chipembedza utachimwa kwambiri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ngati mkulu akukwiyira, usasiye malo ako; chifukwa chifatso chipembedza utachimwa kwambiri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Wolamula akakukwiyira, usachoke pa ntchito yako, pakuti kufatsa kumakonza ngakhale zolakwa zazikulu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ngati wolamulira akukwiyira, usachoke pa ntchito yako; kufatsa kumakonza zolakwa zazikulu.

Onani mutuwo



Mlaliki 10:4
5 Mawu Ofanana  

Munthu wozaza aputa makani; koma wosakwiya msanga atonthoza makangano.


Chipiriro chipembedza mkulu; lilime lofatsa lithyola fupa.


Pali choipa ndachiona pansi pano, ngati kulakwa koyambira ndi mkulu;


Usakangaze kumchokera; usaumirire kanthu koipa; pakuti iyeyo amachita chomwe chimkonda.