Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mlaliki 10:3 - Buku Lopatulika

Inde, poyendanso chitsiru panjira, nzeru yake imthera ndipo angoti kwa onse kuti, Ndine chitsiru.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Inde, poyendanso chitsiru panjira, nzeru yake imthera ndipo angoti kwa onse kuti, Ndine chitsiru.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chitsiru ngakhale chikamayenda mu mseu, zochita zake nzopanda nzeru ndithu, ndipo aliyense amachizindikira kuti nchitsirudi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Chitsiru ngakhale chikamayenda mu msewu, zochita zake ndi zopanda nzeru ndipo chimaonetsa aliyense kuti icho ndi chitsirudi.

Onani mutuwo



Mlaliki 10:3
5 Mawu Ofanana  

Yense wochenjera amachita mwanzeru; koma wopusa aonetsa utsiru.


Wopusa sakondwera ndi kuzindikira; koma kungovumbulutsa za m'mtima mwake.


Milomo ya wopusa ifikitsa makangano; ndipo m'kamwa mwake muputa kukwapulidwa.


Pakuti loto lafika mwakuchuluka ntchito; ndipo mau a chitsiru mwakuchuluka maneno.


m'menemo ayesa nchachilendo kuti simuthamanga nao kufikira kusefukira komwe kwa chitayiko, nakuchitirani mwano;