Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mlaliki 1:7 - Buku Lopatulika

Mitsinje yonse ithira m'nyanja, koma nyanja yosadzala; komwe imukira mitsinjeyo, komweko ibweranso.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mitsinje yonse ithira m'nyanja, koma nyanja yosadzala; komwe imukira mitsinjeyo, komweko ibweranso.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mitsinje yonse imakathira ku nyanja, koma nyanjayo osadzaza. Kumene madzi adachokera amabwereranso komweko.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mitsinje yonse imakathira ku nyanja, koma nyanjayo sidzaza; kumene madziwo amachokera, amabwereranso komweko.

Onani mutuwo



Mlaliki 1:7
4 Mawu Ofanana  

Kulowa kumwera ndi kuzungulira kumpoto zungulirezungulire imaomba mphepo; ibweranso monga mwa mazunguliridwe ake.


Zinthu zonse zilemetsa; munthu sangathe kuzifotokoza; maso sakhuta m'kuona, ndi makutu sakhuta m'kumva.