Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mlaliki 1:5 - Buku Lopatulika

Inde dzuwa lituluka, nililowa, nilifulumira komwe linatulukako.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Inde dzuwa lituluka, nililowa, nilifulumira komwe linatulukako.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Dzuŵa limatuluka, nkukaloŵa, ndipo limapita mwamsanga kumene linatulukira.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Dzuwa limatuluka ndipo dzuwa limalowa ndipo limapita mwamsanga kumene limatulukira.

Onani mutuwo



Mlaliki 1:5
9 Mawu Ofanana  

Pakukhalabe masiku a dziko lapansi, nthawi yakubzala ndi yakukunkha, chisanu ndi mafundi, malimwe ndi msakasa, usana ndi usiku sizidzalekai.


Monga nswala ipuma wefuwefu kukhumba mitsinje; motero moyo wanga upuma wefuwefu kukhumba Inu, Mulungu.


mpaka muvi ukapyoza mphafa yake; amtsata monga mbalame yothamangira msampha; osadziwa kuti adzaononga moyo wake.


Pakuti Yehova atero: Ngati mukhoza kuswa pangano langa la usana ndi pangano langa la usiku, kuti usakhalenso usana ndi usiku, m'nyengo yao;


Dzuwa ndi mwezi zinaima njera mokhala mwao; pa kuunika kwa mivi yanu popita iyo. Pa kung'anipa kwa nthungo yanu yonyezimira.