Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mlaliki 1:4 - Buku Lopatulika

Mbadwo wina upita, mbadwo wina nufika; koma dziko lingokhalabe masiku onse.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mbadwo wina upita, mbadwo wina nufika; koma dziko lingokhalabe masiku onse.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mbadwo wina ukutha, wina ukudza, koma dziko lapansi limakhalapobe losasinthika.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mibado imabwera ndipo mibado imapita, koma dziko lapansi limakhalapobe nthawi zonse.

Onani mutuwo



Mlaliki 1:4
17 Mawu Ofanana  

Ndipo Yakobo anati kwa Farao, Masiku a zaka za ulendo wanga ndi zaka zana limodzi kudza makumi atatu; masiku a zaka za moyo wanga ali owerengeka ndi oipa, sanafikire masiku a zaka za moyo wa makolo anga m'masiku a ulendo wao.


anakhazika dziko lapansi pa maziko ake, silidzagwedezeka kunthawi yonse.


Iwo akukhulupirira Yehova akunga phiri la Ziyoni, losasunthika, likhazikika kosatha.


Pakuti ndani adziwa chomwe chili chabwino kwa munthu ali ndi moyo masiku onse a moyo wake wachabe umene autsiriza ngati mthunzi? Pakuti ndani adzauza munthu chimene chidzaoneka m'tsogolo mwake kunja kuno?


Makolo anu, ali kuti iwowo? Ndi aneneri, akhala ndi moyo kosatha kodi?


Thambo ndi dziko lapansi zidzachoka, koma mau anga sadzachoka ai.


Pomalizira anamwaliranso mkaziyo.