Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mlaliki 1:12 - Buku Lopatulika

Ine Mlaliki ndinali mfumu ya Israele mu Yerusalemu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ine Mlaliki ndinali mfumu ya Israele m'Yerusalemu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ine Mlalikine ndidakhalapo mfumu yolamulira Israele ku Yerusalemu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ine, Mlalikine, ndinali mfumu ya Israeli mu Yerusalemu.

Onani mutuwo



Mlaliki 1:12
4 Mawu Ofanana  

Mau a Mlaliki, mwana wa Davide, mfumu ya mu Yerusalemu.


Chabe zachabetu, ati Mlalikiyo; zonse ndi chabe.


Taonani, ichi ndachipeza, ati Mlalikiyo, m'kuphatikiza chinthu china ndi chinzake, ndikazindikire malongosoledwe ao;