Mika 6:4 - Buku Lopatulika
Pakuti ndinakukwezani kukutulutsani m'dziko la Ejipito, ndi kuombola inu m'nyumba ya ukapolo; ndipo ndinatuma akutsogolereni Mose, Aroni, ndi Miriyamu.
Onani mutuwo
Pakuti ndinakukwezani kukutulutsani m'dziko la Ejipito, ndi kuombola inu m'nyumba ya ukapolo; ndipo ndinatuma akutsogolereni Mose, Aroni, ndi Miriyamu.
Onani mutuwo
Paja Ine ndidakutulutsani ku dziko la Ejipito. Ndidakuwombolani ku dziko laukapololo. Ndipo ndidaachita kutuma Mose, Aroni ndi Miriyamu kuti akutsogolereni.
Onani mutuwo
Ine ndinakutulutsani ku dziko la Igupto ndi kukuwombolani ku nyumba ya ukapolo. Ndinatuma Mose kuti akutsogolereni, pamodzi ndi Aaroni ndi Miriamu.
Onani mutuwo