Mika 6:14 - Buku Lopatulika
Udzadya koma osakhuta; ndi njala yako idzakhala pakati pako; ndipo udzachotsa koma osalanditsa; ndi ichi wachilanditsa ndidzachipereka kulupanga.
Onani mutuwo
Udzadya koma osakhuta; ndi njala yako idzakhala pakati pako; ndipo udzachotsa koma osalanditsa; ndi ichi wachilanditsa ndidzachipereka kulupanga.
Onani mutuwo
Mudzadya, koma simudzakhuta. Njala sidzakuchokani. Mudzakundika zinthu, koma sizidzasungika. Zimene mudzakundika zidzaonongedwa pa nkhondo.
Onani mutuwo
Mudzadya, koma simudzakhuta; mudzakhalabe ndi njala. Mudzasunga zinthu, koma sizidzasungika, chifukwa zimene mudzasunga zidzawonongedwa ndi lupanga.
Onani mutuwo