Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mika 6:11 - Buku Lopatulika

Kodi ndikhoza kuyera ndi miyeso yoipa, ndi thumba la miyala yonyenga?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Kodi ndikhoza kuyera ndi miyeso yoipa, ndi thumba la miyala yonyenga?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kodi ndingathe kulekerera munthu amene ali ndi sikelo zobera anzake ndiponso miyeso yonyenga?

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kodi ndimutenge ngati wosalakwa munthu amene ali ndi sikelo yachinyengo, ndiponso miyeso yabodza mʼthumba lake?

Onani mutuwo



Mika 6:11
9 Mawu Ofanana  

Muyeso wonyenga unyansa Yehova; koma mulingo wamphumphu umsekeretsa.


Mwini muyeso ndi mulingo wolungama ndiye Yehova; ndiyenso anapanga miyala yonse yoyesera ya m'thumba.


Miyeso yosiyana, ndi malichero osiyana, zonse ziwirizi zinyansa Yehova.


Muzikhala nayo miyeso yoona, ndi efa woona, ndi bati loona.


Ndiye Mkanani, m'dzanja lake muli miyeso yonyenga, akonda kusautsa.


Mukhale nacho choyesera choona, miyeso yoona, efa woona, hini woona; Ine ndine Yehova Mulungu wanu, amene ndinakutulutsani m'dziko la Ejipito.


Mwezi wokhala upita liti, kuti tigulitse dzinthu? Ndi Sabata, kuti titsegulire tirigu? Ndi kuchepsa efa, ndi kukulitsa sekeli, ndi kuchenjerera nayo miyeso yonyenga;


Ndipo anati, Uyu ndi uchimo; namgwetsa m'kati mwa efa; naponya ntovu wolemerawo pakamwa pake.


Musamakhala nayo m'thumba mwanu miyala ya miyeso iwiri, waukulu ndi waung'ono.