Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mika 3:10 - Buku Lopatulika

Amanga Ziyoni ndi mwazi, ndi Yerusalemu ndi chisalungamo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Amanga Ziyoni ndi mwazi, ndi Yerusalemu ndi chisalungamo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mumamanga Ziyoni ndi chuma chochipata pakupha anthu, Yerusalemu mumammanga ndi kuipa kwanu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

inu amene mukumanga Ziyoni pokhetsa magazi, ndi Yerusalemu ndi kuyipa kwanu.

Onani mutuwo



Mika 3:10
8 Mawu Ofanana  

Nuziti, Atero Ambuye Yehova, Ndiwo mzinda wokhetsa mwazi pakati pake kuti nthawi yake ifike, nudzipangire mafano udzidetsa nao.


Watha wachifundo m'dziko, palibe woongoka mwa anthu; onsewo alalira mwazi; yense asaka mbale wake ndi ukonde.


Akalonga ake m'kati mwake ndiwo mikango yobangula; oweruza ake ndi mimbulu ya madzulo, sasiya kanthu ka mawa.


Ndipo anthu onse anavomereza, ndi kuti, Mwazi wake uli pa ife ndi pa ana athu.


kapena simuganiza kuti nkokoma kwa inu kuti munthu mmodzi afere anthu, ndi kuti mtundu wonse usaonongeke.