Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 9:25 - Buku Lopatulika

Koma pamene khamulo linatulutsidwa, Iye analowamo, nagwira dzanja lake; ndipo kabuthuko kadauka.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma pamene khamulo linatulutsidwa, Iye analowamo, nagwira dzanja lake; ndipo kabuthuko kadauka.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma onsewo atatulutsidwa, Yesu adaloŵa, nagwira mtsikanayo pa dzanja, iye nkuuka.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Atangowatulutsa anthuwo, analowa mʼnyumba ndipo anagwira dzanja la mtsikanayo ndipo anauka.

Onani mutuwo



Mateyu 9:25
7 Mawu Ofanana  

ndipo anadza namgwira dzanja, namuutsa; ndipo malungo anamleka, ndipo anawatumikira iwo.


Ndipo anagwira dzanja lake la mwana, nanena kwa iye, Talita koumi, ndiko kunena posandulika, Buthu, ndinena ndi iwe, Uka.


Ndipo anamgwira dzanja munthu wakhunguyo, natulukira naye kunja kwa mudzi; ndipo atamthira malovu m'maso mwake, naika manja pa iye, anamfunsa, Uona kanthu kodi?


Koma Yesu anamgwira dzanja lake, namnyamutsa; ndipo anaimirira.


Ndipo Iye anamgwira dzanja lake, naitana, nati, Buthu, tauka.