Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 9:21 - Buku Lopatulika

pakuti analikunena mwa iye yekha, Ngati ndingakhudze chofunda chake chokha ndidzachira.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

pakuti analikunena mwa iye yekha, Ngati ndingakhudze chofunda chake chokha ndidzachira.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mumtima mwake ankaganiza kuti, “Ndikangokhudza ngakhale chovala chake chokhacho, ndichira.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iyeyo anati mwa iye yekha, “Nditangokhudza kasonga ka mkanjo wake, ine ndidzachiritsidwa.”

Onani mutuwo



Mateyu 9:21
6 Mawu Ofanana  

ndipo anampempha Iye, kuti akhudze mphonje yokha ya chovala chake; ndipo onse amene anamkhudza anachiritsidwa.


pakuti adawachiritsa ambiri; kotero kuti onse akukhala nazo zowawa anakanikiza Iye, kuti akamkhudze.


ndi khamu lonse lija linafuna kumkhudza Iye; chifukwa munatuluka mphamvu mwa Iye, nkuchiritsa onsewa.


kotero kuti anamuka nazo kwa odwala nsalu zopukutira ndi za pantchito, zochokera pathupi pake, ndipo nthenda zinawachokera, ndi ziwanda zinatuluka.