Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 9:19 - Buku Lopatulika

Ndipo Yesu ananyamuka namtsata iye, ndi ophunzira ake omwe.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Yesu ananyamuka namtsata iye, ndi ophunzira ake omwe.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamenepo Yesu adanyamuka, namtsatira pamodzi ndi ophunzira ake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yesu ndi ophunzira ake ananyamuka napita naye pamodzi.

Onani mutuwo



Mateyu 9:19
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Yesu ananena naye, Ndifika Ine, ndidzamchiritsa iye.


M'mene Iye analikulankhula nao zinthu zimenezo, onani, anadza munthu mkulu, namgwadira Iye, nanena, Wamwalira tsopanoli mwana wanga wamkazi, komatu mudze muike dzanja lanu pa iye, ndipo adzakhala ndi moyo.


Ndipo onani, mkazi, anali ndi nthenda yachidwalire zaka khumi ndi ziwiri, anadza pambuyo pake, nakhudza mphonje ya chofunda chake;


Yesu ananena nao, Chakudya changa ndicho kuti ndichite chifuniro cha Iye amene anandituma Ine, ndi kutsiriza ntchito yake.


za Yesu wa ku Nazarete, kuti Mulungu anamdzoza Iye ndi Mzimu Woyera ndi mphamvu; amene anapitapita nachita zabwino, nachiritsa onse osautsidwa ndi mdierekezi, pakuti Mulungu anali pamodzi ndi Iye.