Ndipo onani, panauka namondwe wamkulu panyanja, kotero kuti ngalawa inafundidwa ndi mafunde: koma Iye anali m'tulo.
Mateyu 8:23 - Buku Lopatulika Ndipo pamene Iye atalowa m'ngalawa, ophunzira ake anamtsata Iye. Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014 Ndipo pamene Iye atalowa m'ngalawa, ophunzira ake anamtsata Iye. Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa Yesu adaloŵa m'chombo, ndipo ophunzira ake adatsagana naye. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Iye atalowa mʼbwato, ophunzira ake anamutsatira. |
Ndipo onani, panauka namondwe wamkulu panyanja, kotero kuti ngalawa inafundidwa ndi mafunde: koma Iye anali m'tulo.
Ndipo anayankha, nati kwa iwo, Mukani, muuze Yohane zimene mwaziona, nimwazimva; anthu akhungu alandira kuona kwao, opunduka miyendo ayenda, akhate akonzedwa, ogontha akumva, akufa aukitsidwa, kwa aumphawi ulalikidwa Uthenga Wabwino.