Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 7:20 - Buku Lopatulika

Inde chomwecho pa zipatso zao mudzawazindikira iwo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Inde chomwecho pa zipatso zao mudzawazindikira iwo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Choncho mudzaŵadziŵira zochita zao.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Momwemonso, ndi zipatso zawo iwo mudzawazindikira.

Onani mutuwo



Mateyu 7:20
5 Mawu Ofanana  

Ukakoma mtengo, chipatso chake chomwe chikoma; ukaipa mtengo, chipatso chake chomwe chiipa; pakuti ndi chipatso chake mtengo udziwika.


Mudzawazindikira ndi zipatso zao. Kodi atchera mphesa paminga, kapena nkhuyu pamtula?


Pakuti mtengo uliwonse uzindikirika ndi chipatso chake. Pakuti anthu samatchera nkhuyu paminga, kapena pamtungwi samatchera mphesa.


Ndipo tsopano ndinena ndi inu, Lekani anthu amenewa, nimuwalole akhale; pakuti ngati uphungu umene kapena ntchito iyi ichokera kwa anthu, idzapasuka;


Kodi mkuyu ukhoza kubala azitona, abale anga, kapena mpesa kubala nkhuyu? Kotero madzi amchere sangathe kutulutsa okoma.