Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 6:29 - Buku Lopatulika

koma ndinena kwa inu, kuti angakhale Solomoni mu ulemerero wake wonse sanavale monga limodzi la amenewa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

koma ndinena kwa inu, kuti angakhale Solomoni mu ulemerero wake wonse sanavale monga limodzi la amenewa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Komatu kunena zoona, ngakhale mfumu Solomoni yemwe, mu ulemerero wake wonse, sankavala zokongola kulingana ndi limodzi lomwe mwa maluŵa ameneŵa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndikukuwuzani kuti angakhale Solomoni mu ulemerero wake sanavale mofanana ndi limodzi la maluwa amenewa.

Onani mutuwo



Mateyu 6:29
5 Mawu Ofanana