Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 6:17 - Buku Lopatulika

Koma iwe, posala kudya, dzola mutu wako, ndi kusamba nkhope yako:

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma iwe, posala kudya, dzola mutu wako, ndi kusamba nkhope yako:

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma iwe, pamene ukusala zakudya, samba m'maso nkudzola mafuta kumutu,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma pamene ukusala kudya, samba mʼmaso nudzole mafuta kumutu,

Onani mutuwo



Mateyu 6:17
5 Mawu Ofanana  

Pamenepo Davide ananyamuka pansi, nasamba, nadzola, nasintha zovala; nafika kunyumba ya Yehova, napembedza; pamenepo anafika kunyumba yake; ndipo powauza anamuikira chakudya, nadya iye.


Ndipo Yowabu anatumiza ku Tekowa, natenga kumeneko mkazi wanzeru, nanena naye, Ukokomezeke monga mfedwa, nuvale zovala za pamaliro, osadzola mafuta, koma ukhale ngati munthu wamkazi wakulira akufa nthawi yaikulu.


Zovala zako zikhale zoyera masiku onse; mutu wako usasowe mafuta.


Usambe tsono, nudzole, nuvale zovala zako, nutsikire popunthirapo, koma usadziwike naye munthuyo, koma atatha kudya ndi kumwa ndiko.