Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 6:15 - Buku Lopatulika

Koma ngati simukhululukira anthu zolakwa zao, Atate wanunso sadzakhululukira zolakwa zanu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma ngati simukhululukira anthu zolakwa zao, Atate wanunso sadzakhululukira zolakwa zanu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma ngati simukhululukira anthu machimo ao, Atate anunso sadzakukhululukirani machimo anu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma ngati inu simukhululukira anthu zolakwa zawo, Atate anunso sadzakukhululukirani machimo anu.

Onani mutuwo



Mateyu 6:15
4 Mawu Ofanana  

Chomwechonso Atate wanga a Kumwamba adzachitira inu, ngati inu simukhululukira yense mbale wake ndi mitima yanu.


Odala ali akuchitira chifundo; chifukwa adzalandira chifundo.


Pakuti ngati mukhululukira anthu zolakwa zao adzakhululukira inunso Atate wanu wa Kumwamba.