Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 6:11 - Buku Lopatulika

Mutipatse ife lero chakudya chathu chalero.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Mutipatse ife lero chakudya chathu chalero.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mutipatse ife lero chakudya chathu chamasikuwonse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mutipatse chakudya chathu chalero.

Onani mutuwo



Mateyu 6:11
12 Mawu Ofanana  

Sindinabwerera kusiya malamulo a pa milomo yake; ndasungitsa mau a pakamwa pake koposa lamulo langalanga.


Misona ya mkango isowa nimva njala, koma iwo akufuna Yehova sadzasowa kanthu kabwino.


Mundichotsere kutali zachabe ndi mabodza; musandipatse umphawi, ngakhale chuma, mundidyetse zakudya zondiyenera;


iye adzakhala pamsanje; malo ake ochinjikiza adzakhala malinga amiyala; chakudya chake chidzapatsidwa kwa iye; madzi ake adzakhala chikhalire.


Koma Iye anayankha nati, Kwalembedwa, Munthu sadzakhala ndi moyo ndi mkate wokha, koma ndi mau onse akutuluka m'kamwa mwa Mulungu.


tipatseni ife tsiku ndi tsiku chakudya cha patsiku.


Koma oterewa tiwalamulira ndi kuwadandaulira mwa Ambuye Yesu Khristu, kuti agwire ntchito pokhala chete, nadye chakudya cha iwo okha.


koma pokhala nazo zakudya ndi zofunda, zimene zitikwanire.


Pamenepo ananyamuka iyeyu ndi apongozi ake kuti abwerere kuchoka m'dziko la Mowabu; pakuti adamva m'dziko la Mowabu kuti Yehova adasamalira anthu ake ndi kuwapatsa chakudya.