Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 5:27 - Buku Lopatulika

Munamva kuti kunanenedwa, Usachite chigololo;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Munamva kuti kunanenedwa, Usachite chigololo;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

“Mudamva kuti anthu akale aja adaaŵalamula kuti, ‘Usachite chigololo.’

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

“Munamva kuti kunanenedwa kuti, ‘Usachite chigololo.’

Onani mutuwo



Mateyu 5:27
10 Mawu Ofanana  

Usachite chigololo.


Wochita chigololo ndi mkazi alibe nzeru; wofuna kuononga moyo wakewake ndiye amatero.


Usagona naye mkazi wa mnansi wako, kudetsedwa naye limodzi.


Munthu akachita chigololo ndi mkazi wa mwini, popeza wachita chigololo ndi mkazi wa mnansi wake, awaphe ndithu, mwamuna ndi mkazi onse awiri.


Munamva kuti kunanenedwa kwa iwo akale, Usaphe; koma yense wakupha adzakhala wopalamula mlandu:


Ndiponso, munamva kuti kunanenedwa kwa iwo akale, Usalumbire konama, koma udzapereka kwa Ambuye zolumbira zako:


Munamva kuti kunanenedwa, Diso kulipa diso, ndi dzino kulipa dzino:


Munamva kuti kunanenedwa, Uzikondana ndi mnansi wako, ndi kumuda mdani wako: