Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 4:20 - Buku Lopatulika

Ndipo iwo anasiya pomwepo makokawo, namtsata Iye.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo iwo anasiya pomwepo makokawo, namtsata Iye.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pomwepo iwo adasiya makoka ao, namamtsatadi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Nthawi yomweyo anasiya makoka awo namutsata Iye.

Onani mutuwo



Mateyu 4:20
10 Mawu Ofanana  

Ndipo anabwerera panali iye uja, natengako ng'ombe ziwiri, nazipha, naphikira nyama yake ndi zipangizo za zochitira nazo ng'ombe, napatsa anthu adye. Atatero, ananyamuka, natsata Eliya, namtumikira.


Ndinafulumira, osachedwa, kusamalira malamulo anu.


Iye wakukonda atate wake, kapena amake koposa Ine, sayenera Ine, ndipo iye wakukonda mwana wake wamwamuna, kapena wamkazi koposa Ine, sayenera Ine.


Pomwepo Petro anayankha, nati kwa Iye, onani, ife tinasiya zonse ndi kutsata Inu; nanga tsono tidzakhala ndi chiyani?


Ndipo Iye ananena nao, Tiyeni pambuyo panga, ndidzakusandutsani asodzi a anthu.


Ndipo popitirirapo Iye anaona abale ena awiri, Yakobo mwana wa Zebedeo, ndi Yohane mbale wake, m'ngalawa, pamodzi ndi Zebedeo atate wao, analikusoka makoka ao; ndipo anaitana iwo.


Ndipo m'mene iwo anakocheza ngalawa zao pamtunda, anasiya zonse, namtsata Iye.


kuti avumbulutse Mwana wake mwa ine, kuti ndimlalikire Iye mwa amitundu; pomwepo sindinafunsane ndi thupi ndi mwazi: