Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 28:4 - Buku Lopatulika

ndipo ndi kuopsa kwake alondawo ananthunthumira, nakhala ngati anthu akufa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo ndi kuopsa kwake alondawo ananthunthumira, nakhala ngati anthu akufa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamenepo alonda aja adachita mantha nayamba kunjenjemera, nkungoti gwa ngati anthu akufa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Alondawo anachita naye mantha kwambiri kotero kuti ananjenjemera ndi kuwuma ngati akufa.

Onani mutuwo



Mateyu 28:4
10 Mawu Ofanana  

Anandidzera mantha ndi kunjenjemera, nanthunthumira nako mafupa anga onse.


Pomwepo anagwidwa nako kunthunthumira; anamva chowawa, ngati wam'chikuta.


Ndipo ine Daniele ndekha ndinaona masomphenyawo; pakuti anthu anali nane sanaone masomphenyawo; koma kunawagwera kunjenjemera kwakukulu, nathawa kubisala.


Ndipo pamene iwo analikupita, onani, ena a alonda anafika kumzinda, nauza ansembe aakulu zonse zimene zinachitidwa.


Kuonekera kwake kunali ngati mphezi, ndi chovala chake choyeretsa ngati matalala;


Koma mngelo anayankha, nati kwa akaziwo, Musaope inu; pakuti ndidziwa inu mulikufuna Yesu, amene anapachikidwa.


Ndipo mdindo anaitanitsa nyali, natumphira m'kati, alinkunthunthumira ndi mantha, nagwa pamaso pa Paulo ndi Silasi,


Ndipo pamene ndinamuona Iye, ndinagwa pa mapazi ake ngati wakufa; ndipo anaika dzanja lake lamanja pa ine, nati, Usaope, Ine ndine Woyamba ndi Wotsiriza,