Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 28:11 - Buku Lopatulika

Ndipo pamene iwo analikupita, onani, ena a alonda anafika kumzinda, nauza ansembe aakulu zonse zimene zinachitidwa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pamene iwo analikupita, onani, ena a alonda anafika kumzinda, nauza ansembe aakulu zonse zimene zinachitidwa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene akazi aja ankapita, ena mwa alonda aja adakafika ku mzinda, nakasimbira akulu a ansembe zonse zimene zidaachitika.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Amayi aja akupita, ena mwa alonda aja anapita ku mzinda nafotokozera akulu a ansembe zonse zimene zinachitika.

Onani mutuwo



Mateyu 28:11
3 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene anasonkhana pamodzi ndi akulu, anakhala upo, napatsa asilikaliwo ndalama zambiri,


ndipo ndi kuopsa kwake alondawo ananthunthumira, nakhala ngati anthu akufa.