Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 27:61 - Buku Lopatulika

Ndipo Maria wa Magadala anali pamenepo, ndi Maria winayo, anakhala pansi popenyana ndi mandawo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Maria wa Magadala anali pamenepo, ndi Maria winayo, anakhala pansi popenyana ndi mandawo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Maria wa ku Magadala ndi Maria wina uja anali pomwepo atakhala pansi kuyang'anana ndi mandawo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mariya wa Magadala ndi Mariya wina anakhala pansi moyangʼanizana ndi mandawo.

Onani mutuwo



Mateyu 27:61
2 Mawu Ofanana  

mwa iwo amene munali Maria wa Magadala, ndi Maria amake wa Yakobo, ndi wa Yosefe, ndi amake wa ana a Zebedeo.


Ndipo popita tsiku la Sabata, mbandakucha, tsiku lakuyamba la sabata, anadza Maria wa Magadala, ndi Maria winayo, kudzaona manda.