Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 27:47 - Buku Lopatulika

Ndipo ena a iwo akuimirira komweko, pamene anamva, ananena, Uyo aitana Eliya.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ena a iwo akuimirira komweko, pamene anamva, ananena, Uyo aitana Eliya.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Atamva mauwo, ena amene adaaimirira pamenepo adati, “Munthuyu akuitana Eliya.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ena a oyimirira pamalopo atamva izi anati, “Akuyitana Eliya.”

Onani mutuwo



Mateyu 27:47
5 Mawu Ofanana  

Taonani, ndidzakutumizirani Eliya mneneri lisanadze tsiku lalikulu ndi loopsa la Yehova.


Ndipo ngati mufuna kulandira, uyu ndiye Eliya amene amati akudza.


Ndipo poyandikira ora lachisanu ndi chinai, Yesu anafuula ndi mau aakulu, kunena, Eli, Eli, lama sabakitani? ndiko kunena kuti, Mulungu wanga, Mulungu wanga, mwandisiyiranji Ine?


Ndipo pomwepa mmodzi wa iwo anathamanga, natenga chinkhupule, nachidzaza ndi vinyo wosasa, nachiika pabango, namwetsa Iye.