Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 27:20 - Buku Lopatulika

Koma ansembe aakulu ndi akulu anapangira anthu kuti apemphe Barabasi, koma kuti aononge Yesu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma ansembe aakulu ndi akulu anapangira anthu kuti apemphe Barabasi, koma kuti aononge Yesu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Akulu a ansembe ndi akulu a Ayuda adayamba kukakamiza anthu kupempha Pilato kuti amasule Barabasi, ndipo kuti Yesu aphedwe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma akulu a ansembe ndi akuluakulu ananyengerera gulu la anthu kuti apemphe Baraba ndi kuti Yesu aphedwe.

Onani mutuwo



Mateyu 27:20
10 Mawu Ofanana  

Ndipo panali, pamene Yeremiya anatha kunena mau onse amene Yehova anamuuza iye kuti anene kwa anthu onse, ansembe ndi aneneri ndi anthu onse anamgwira iye, ndi kuti, Udzafa ndithu.


Koma kazembe anati kwa iwo, Mufuna kuti ndikumasulireni uti wa awa awiri? Ndipo iwo anati, Barabasi.


Koma ansembe aakulu anasonkhezera khamulo, kuti makamaka awamasulire Barabasi.


Pomwepo anafuulanso, nanena, Si uyu, koma Barabasi. Koma Barabasi anali wachifwamba.


Ndipo anafotokozera m'sunagoge masabata onse, nakopa Ayuda ndi Agriki.