Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 27:16 - Buku Lopatulika

Ndipo pa nthawi yomweyo anali ndi wandende wodziwika, dzina lake Barabasi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pa nthawi yomweyo anali ndi wandende wodziwika, dzina lake Barabasi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pa nthaŵi imeneyo panali mkaidi wina wodziŵika, dzina lake Barabasi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pa nthawiyo anali ndi wamʼndende woyipa kwambiri dzina lake Baraba.

Onani mutuwo



Mateyu 27:16
9 Mawu Ofanana  

Ndipo pa chikondwerero kazembe adazolowera kumasulira anthu mmodzi wandende, amene iwo anafuna.


Chifukwa chake pamene anasonkhana, Pilato ananena kwa iwo, Mufuna kuti ndikumasulireni yani? Barabasi kodi, kapena Yesu, wotchedwa Khristu?


Ndipo analipo wina dzina lake Barabasi, womangidwa pamodzi ndi opanduka, amene anapha munthu mumpanduko.


Ndipo anawamasulira amene adaponyedwa m'ndende chifukwa cha mpanduko ndi kupha munthu, amene iwo anampempha; koma anapereka Yesu mwa chifuniro chao.


Pomwepo anafuulanso, nanena, Si uyu, koma Barabasi. Koma Barabasi anali wachifwamba.


Koma inu munakaniza Woyera ndi Wolungamayo, ndipo munapempha kuti munthu wambanda apatsidwe kwa inu,


amene ngakhale adziwa kuweruza kwake kwa Mulungu, kuti iwo amene achita zotere ayenera imfa, azichita iwo okha, ndiponso avomerezana ndi iwo akuzichita.


Moni kwa Androniko ndi Yunia, anansi anga, ndi andende anzanga, amene ali omveka mwa atumwi, amenenso ananditsogolera ine mwa Khristu.