Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 27:10 - Buku Lopatulika

ndipo anazipereka kugula munda wa woumba mbiya, monga anandilamulira ine Ambuye.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo anazipereka kugula munda wa woumba mbiya, monga anandilamulira ine Ambuye.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

nagulira munda wa mmisiri wa mbiya, monga momwe Ambuye adaandilamulira.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo anazigwiritsa ntchito kugula munda wa wowumba mbiya monga mmene Ambuye anandilamulira ine.”

Onani mutuwo



Mateyu 27:10
2 Mawu Ofanana  

Ndipo ndinanena nao, Chikakomera inu, ndipatseni mphotho yanga; ngati iai, lekani. Ndipo anayesa mphotho yanga, kulemera kwake masekeli a siliva makumi atatu.


Ndipo Yehova anati kwa ine, Kaziponye kwa woumba mbiya, mtengo wake wokometsetsa anandiyesawo. Ndipo ndinatenga masekeli makumi atatu a siliva, ndi kuziponya kwa woumba mbiya, m'nyumba ya Yehova.