Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 26:68 - Buku Lopatulika

nati, Utilote ife, Khristu Iwe; wakumenya Iwe ndani?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

nati, Utilote ife, Khristu Iwe; wakumenya Iwe ndani?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

nkumanena kuti, “Iwe Mpulumutsi wolonjezedwa uja, nanga sindiwe mneneri? Lota, wakumenya ndani?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo anati, “Tanenera kwa ife, Khristu. Wakumenya ndani?”

Onani mutuwo



Mateyu 26:68
11 Mawu Ofanana  

Pomwepo iwo anathira malovu pankhope pake, nambwanyula Iye; ndipo ena anampanda khofu,


Ndipo ena anayamba kumthira malovu Iye, ndi kuphimba nkhope yake, ndi kumbwanyula, ndi kunena naye, Lota; ndipo anyamatawo anampanda Iye khofu.


Ndipo kunali, pakukondwera mitima yao, anati, Kaitaneni Samisoni, atisewerere. Naitana Samisoni m'kaidi; nasewera iye pamaso pao; ndipo anamuka iye pakati pa mizati.