Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 26:66 - Buku Lopatulika

muganiza bwanji? Iwo anayankha nati, Ali woyenera kumupha.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

muganiza bwanji? Iwo anayankha nati, Ali woyenera kumupha.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndiye inu mukuganiza bwanji?” Iwo aja adayankha kuti, “Ayenera kuphedwa.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mukuganiza bwanji?” Iwo anayankha kuti, “Ayenera kuphedwa!”

Onani mutuwo



Mateyu 26:66
8 Mawu Ofanana  

Ichi chikhale mphotho ya otsutsana nane yowapatsa Yehova, ndi ya iwo akunenera choipa moyo wanga.


Ndipo ansembe ndi aneneri ananena kwa akulu ndi kwa anthu onse, kuti, Munthu uyu ayenera kufa; pakuti wanenera mzinda uwu monga mwamva ndi makutu anu.


Ayuda anamyankha iye, Tili nacho chilamulo ife, ndipo monga mwa chilamulocho ayenera kufa, chifukwa anadziyesera Mwana wa Mulungu.


Ndiye yani wa aneneri makolo anu sanamzunze? Ndipo anawapha iwo amene anaonetseratu za kudza kwake kwa Wolungamayo; wa Iye amene mwakhala tsopano akumpereka ndi akumupha;


Munthu akakhala nalo tchimo loyenera imfa, kuti amuphe, ndipo wampachika;


Munamtsutsa, munapha wolungamayo, iye sakaniza inu.