Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 26:60 - Buku Lopatulika

koma sanaupeze zingakhale mboni zonama zambiri zinadza. Koma pambuyo pake anadza awiri,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

koma sanaupeze zingakhale mboni zonama zambiri zinadza. Koma pambuyo pake anadza awiri,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma sadaupeze ngakhale padaabwera mboni zambiri zabodza. Potsiriza padabwera anthu aŵiri.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma sanathe kupeza uliwonse, angakhale kuti mboni zambiri zabodza zinapezeka. Pomalizira mboni ziwiri zinabwera patsogolo.

Onani mutuwo



Mateyu 26:60
7 Mawu Ofanana  

Musandipereke ku chifuniro cha akundisautsa, chifukwa zinandiukira mboni zonama ndi iwo akupumira zachiwawa.


Mboni za chiwawa ziuka, zindifunsa zosadziwa ine.


Mboni imodzi isamaukira munthu pa mphulupulu iliyonse, kapena tchimo lililonse adalichimwa; pakamwa pa mboni ziwiri, kapena pakamwa pa mboni zitatu mlandu utsimikizike.


mau olama osatsutsika; kuti iye wakutsutsana achite manyazi, posakhala nako kanthu koipa kakutinenera ife.


ndi kukhala nacho chikumbumtima chabwino, kuti umo akunenerani, iwo akunenera konama mayendedwe anu abwino mu Khristu akachitidwe manyazi.