Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 26:20 - Buku Lopatulika

Ndipo pakufika madzulo, Iye analinkukhala pachakudya pamodzi ndi ophunzira khumi ndi awiri;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pakufika madzulo, Iye analinkukhala pachakudya pamodzi ndi ophunzira khumi ndi awiri;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kutada, Yesu ndi ophunzira ake khumi ndi aŵiri aja adakhala pamodzi nkumadya.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kutada, Yesu ndi ophunzira ake khumi ndi awiriwo anakhala pa tebulo nʼkumadya.

Onani mutuwo



Mateyu 26:20
6 Mawu Ofanana  

Ndipo muziidya chotero: okwinda m'chuuno, nsapato zanu pa mapazi anu ndodo yanu m'dzanja lanu, ndipo muziidya msanga; ndiye Paska wa Yehova.


Pokhala mfumu podyera pake, narido wanga ananunkhira.


Ndipo ophunzira anachita monga Yesu anawauza, nakonza Paska.


Yesu m'mene adanena izi, anavutika mumzimu, nachita umboni, nati, Indetu, indetu, ndinena ndi inu, kuti mmodzi wa inu adzandipereka Ine.