Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 26:19 - Buku Lopatulika

Ndipo ophunzira anachita monga Yesu anawauza, nakonza Paska.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo ophunzira anachita monga Yesu anawauza, nakonza Paska.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ophunzira aja adapita nakachita zomwe Yesu adaaŵauza, nakakonzadi za phwando la Paska.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamenepo ophunzira ake anachita monga momwe Yesu anawawuzira ndipo anakonza Paska.

Onani mutuwo



Mateyu 26:19
7 Mawu Ofanana  

Ndipo ophunzirawo anamuka, nachita monga Yesu anawauza;


Nati Iye, Mukani kumzinda kwa munthu wina wake, mukati kwa Iye, Mphunzitsi anena, Nthawi yanga yayandikira; ndidzadya Paska kwanu pamodzi ndi ophunzira anga.


Ndipo pakufika madzulo, Iye analinkukhala pachakudya pamodzi ndi ophunzira khumi ndi awiri;


Muli abwenzi anga inu, ngati muzichita zimene ndikulamulani inu.


Amake ananena kwa atumiki, Chimene chilichonse akanena kwa inu, chitani.