Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 24:41 - Buku Lopatulika

awiri adzakhala opera pamphero; mmodzi adzatengedwa, ndi wina adzasiyidwa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

awiri adzakhala opera pamphero; mmodzi adzatengedwa, ndi wina adzasiyidwa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Azimai aŵiri adzakhala akusinja, mmodzi adzamtenga, winayo nkumusiya.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Amayi awiri adzakhala akusinja pa mtondo; wina adzatengedwa ndi wina adzatsala.

Onani mutuwo



Mateyu 24:41
5 Mawu Ofanana  

ndipo ana oyamba a m'dziko la Ejipito adzafa, kuyambira mwana woyamba wa Farao wokhala pa mpando wachifumu wake, kufikira mwana woyamba wa mdzakazi wokhala pa miyala yopera; ndi ana onse oyamba a zoweta.


Tenga mipero, nupere ufa; chotsa chophimba chako, vula chofunda, kwinda m'mwendo, oloka mitsinje.


Pomwepo adzakhala awiri m'munda; mmodzi adzatengedwa, ndi wina adzasiyidwa:


Padzakhala akazi awiri akupera pamodzi, mmodzi adzatengedwa, ndi wina adzasiyidwa.


Munthu asalandire chikole mphero, ngakhale mwanamphero, popeza alandirapo chikole moyo wa munthu.