Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 24:40 - Buku Lopatulika

Pomwepo adzakhala awiri m'munda; mmodzi adzatengedwa, ndi wina adzasiyidwa:

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pomwepo adzakhala awiri m'munda; mmodzi adzatengedwa, ndi wina adzasiyidwa:

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pa nthaŵi imeneyo anthu aŵiri adzakhala ali m'munda, mmodzi adzamtenga, winayo nkumusiya.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Amuna awiri adzakhala mʼmunda; wina adzatengedwa ndi wina adzatsala.

Onani mutuwo



Mateyu 24:40
8 Mawu Ofanana  

ndipo iwo sanadziwe kanthu, kufikira kumene chigumula chinadza, chinapululutsa iwo onse, kotero kudzakhala kufika kwake kwa Mwana wa Munthu.


awiri adzakhala opera pamphero; mmodzi adzatengedwa, ndi wina adzasiyidwa.


Pakuti akusiyanitsa iwe ndani? Ndipo uli nacho chiyani chosati wachilandira? Koma ngati wachilandira udzitamanda bwanji, monga ngati sunachilandire?


ndipo sanalekerere dziko lapansi lakale, koma anasunga Nowa mlaliki wa chilungamo, ndi anzake asanu ndi awiri, pakulitengera dziko la osapembedza chigumula;