Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 24:25 - Buku Lopatulika

Chifukwa chake akanena kwa inu,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Chifukwa chake akanena kwa inu, Onani, Iye ali m'chipululu; musamukeko.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mvetsetsani, Ine ndiye ndakuuziranitu zimenezi.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Onani, ndakuwuzani izi nthawi isanafike.

Onani mutuwo



Mateyu 24:25
9 Mawu Ofanana  

Taonani, Ine ndikutumizani inu monga nkhosa pakati pa mimbulu; chifukwa chake khalani ochenjera monga njoka, ndi oona mtima monga nkhunda.


chifukwa Akhristu onama adzauka, ndi aneneri onama nadzaonetsa zizindikiro zazikulu ndi zozizwa: kotero kuti akanyenge, ngati nkotheka, osankhidwa omwe. Onani ndakuuziranitu pasadafike.


Onani, Iye ali m'chipululu; musamukeko. Onani, ali m'zipinda; musavomereze.


Kudzakhala kwa inu ngati umboni.


Izi ndalankhula ndi inu kuti mungakhumudwitsidwe.


Ndinanena kale, ndipo ndinena ndisanafikeko, monga pamene ndinali pomwepo kachiwiri kaja, pokhala ine palibe, kwa iwo adachimwa kale ndi kwa onse otsala, kuti, ngati ndidzanso sindidzawaleka;