Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 24:18 - Buku Lopatulika

ndi iye wa m'munda asabwere kutenga chofunda chake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi iye wa m'munda asabwere kutenga chofunda chake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yemwe ali ku munda, asabwererenso ku nyumba kuti akatenge mwinjiro.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Yemwe ali ku munda asapite kukatenga mkanjo wake.

Onani mutuwo



Mateyu 24:18
4 Mawu Ofanana  

Nanena naye mfumu, Ufunanji? Nati iye, Mnzanga uyu ananena ndi ine, Tenga mwana wako timudye lero, ndi mwana wanga timudye mawa.


iye ali pamwamba pa tsindwi, asatsikire kunyamula za m'nyumba mwake;


Koma tsoka ali nalo iwo akukhala ndi pakati, ndi akuyamwitsa ana m'masiku awo!


Tsikulo iye amene adzakhala pamwamba pa tsindwi, ndi akatundu ake m'nyumba, asatsike kuwatenga; ndipo iye amene ali m'munda modzimodzi asabwere ku zake za m'mbuyo.