Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 24:16 - Buku Lopatulika

pomwepo iwo ali mu Yudeya athawire kumapiri:

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

pomwepo iwo ali m'Yudeya athawire kumapiri:

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamenepo amene ali ku Yudeya athaŵire ku mapiri.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamenepo amene ali ku Yudeya athawire ku mapiri.

Onani mutuwo



Mateyu 24:16
11 Mawu Ofanana  

Wochenjera aona zoipa, nabisala; koma achibwana angopitirira, nalipitsidwa.


Ndipo ichi chidzakhala chizindikiro cha kwa inu, ati Yehova, chakuti Ine ndidzakulangani m'malo muno, kuti mudziwe kuti mau anga adzatsimikizidwatu akuchitireni inu zoipa.


Ananu a Benjamini, pulumukani pothawa pakati pa Yerusalemu, ombani lipenga mu Tekowa, kwezani chizindikiro mu Betehakeremu; pakuti chaoneka choipa chotuluka m'mpoto ndi kuononga kwakukulu.


Ndipo pa kubadwa kwake kwa Yesu mu Betelehemu wa Yudeya m'masiku a Herode mfumu, onani, Anzeru a kum'mawa anafika ku Yerusalemu,


Chifukwa chake m'mene mukadzaona chonyansa cha kupululutsa, chimene chidanenedwa ndi Daniele mneneri, chitaima m'malo oyera (iye amene awerenga m'kalata azindikire)


iye ali pamwamba pa tsindwi, asatsikire kunyamula za m'nyumba mwake;


Ndi chikhulupiriro Nowa, pochenjezedwa ndi Mulungu za zinthu zisanapenyeke, ndi pochita mantha, anamanga chingalawa cha kupulumutsiramo iwo a m'nyumba yake; kumene anatsutsa nako dziko lapansi, nakhala wolowa nyumba wa chilungamo chili monga mwa chikhulupiriro.