Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 23:6 - Buku Lopatulika

nakonda malo a ulemu pamaphwando, ndi mipando ya ulemu m'masunagoge,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

nakonda malo a ulemu pamaphwando, ndi mipando ya ulemu m'masunagoge,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Amakonda malo olemekezeka pa maphwando ndiponso mipando yaulemu kwambiri ku nyumba zamapemphero.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Amakonda malo aulemu pa maphwando ndi malo ofunika kwambiri mʼmasunagoge.

Onani mutuwo



Mateyu 23:6
9 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye anati kwa iye, Ufuna chiyani? Iye ananena, Lamulirani kuti ana anga awiri amenewa adzakhale, wina ku dzanja lanu lamanja, ndi wina kulamanzere, mu ufumu wanu.


M'chikondano cha anzanu wina ndi mnzake mukondane ndi chikondi chenicheni; mutsogolerane ndi kuchitira wina mnzake ulemu;


Ndalemba kanthu kwa Mpingo; komatu Diotrefe uja, wofuna kukhala wamkulu wa iwo, satilandira ife.