Ndipo pamene Afarisi anasonkhana, Yesu anawafunsa,
Afarisi atasonkhana pamodzi, Yesu adaŵafunsa funso.
Afarisi atasonkhana pamodzi, Yesu anawafunsa kuti,
Pomwepo Afarisi anamuka, nakhala upo wakumkola Iye m'kulankhula kwake.
Koma Afarisi, pakumva kuti Iye anatontholetsa Asaduki, anasonkhana.