Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 22:40 - Buku Lopatulika

Pa malamulo awa awiri mpokolowekapo chilamulo chonse ndi aneneri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pa malamulo awa awiri mpokolowekapo chilamulo chonse ndi aneneri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Malamulo onse a Mose ndiponso zonse zimene aneneri adaphunzitsa zagona pa malamulo aŵiriŵa.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Malamulo onse ndi aneneri zakhazikika pa malamulo awiriwa.”

Onani mutuwo



Mateyu 22:40
9 Mawu Ofanana  

Chifukwa chake zinthu zilizonse mukafuna kuti anthu achitire inu, inunso muwachitire iwo zotero; pakuti icho ndicho chilamulo ndi aneneri.


Chifukwa chilamulo chinapatsidwa mwa Mose; chisomo ndi choonadi zinadza mwa Yesu Khristu.


Pakuti ili, Usachite chigololo, Usaphe, Usabe, Usasirire, ndipo lingakhale lamulo lina lililonse, limangika pamodzi m'mau amenewa, kuti, Uzikonda mnzako monga udzikonda iwe wekha.


Pakuti mau amodzi akwaniritsa chilamulo chonse ndiwo; Uzikonda mnzako monga udzikonda iwe mwini.


koma chitsirizo cha chilamuliro ndicho chikondi chochokera mu mtima woyera ndi m'chikumbu mtima chokoma ndi chikhulupiriro chosanyenga;


Koma ngati muchita chikwanirire lamulolo lachifumu, monga mwa malembo, Uzikonda mnzako monga udzikonda wekha, muchita bwino: