Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 22:34 - Buku Lopatulika

Koma Afarisi, pakumva kuti Iye anatontholetsa Asaduki, anasonkhana.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma Afarisi, pakumva kuti Iye anatontholetsa Asaduki, anasonkhana.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Afarisi atamva kuti Yesu adatsutsa Asaduki, adasonkhana.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pakumva kuti Yesu anawakhalitsa chete Asaduki, Afarisi anasonkhana pamodzi.

Onani mutuwo



Mateyu 22:34
10 Mawu Ofanana  

Ndipo Afarisi anatuluka, nakhala upo womchitira Iye mwa kumuononga.


Ndipo iye pakuona ambiri a Afarisi ndi a Asaduki akudza ku ubatizo wake, anati kwa iwo, Obadwa a njoka inu, ndani anakulangizani kuthawa mkwiyo ulinkudza?


Ndipo taonani, wachilamulo wina anaimirira namuyesa Iye, nanena, Mphunzitsi, ndidzalowa moyo wosatha ndi kuchita chiyani?