Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Mateyu 22:26 - Buku Lopatulika

chimodzimodzi wachiwiri, ndi wachitatu, kufikira wachisanu ndi chiwiri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

chimodzimodzi wachiwiri, ndi wachitatu, kufikira wachisanu ndi chiwiri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chimodzimodzinso wachiŵiri ndi wachitatu, mpaka wachisanu ndi chiŵiri.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Izi zinachitikiranso mʼbale wa chiwiri ndi wachitatu mpaka wachisanu ndi chiwiri.

Onani mutuwo



Mateyu 22:26
4 Mawu Ofanana  

Asumwa, sayankhanso, Anawathera mau.


Ndipo anatumiza kwa Iye ophunzira ao, pamodzi ndi Aherode, amene ananena, Mphunzitsi, tidziwa kuti muli woona, ndipo muphunzitsa njira ya Mulungu moona ndithu, ndipo simusamala munthu aliyense; pakuti simuyang'anira pa nkhope ya anthu.


Tsono panali ndi ife abale asanu ndi awiri; ndipo wakuyamba anakwatira, namwalira wopanda mbeu, nasiyira mphwake mkazi wake;


Ndipo pomalizira anamwaliranso mkaziyo.